Kuti tilandire mokwanira Mulungu amene amatsogolera anthu ku ufumu wa kumwamba, tiyenera kumvetsetsa kuti chizindikiro chodziwira Khristu Wobwera Kachiwiri, Muzu wa Davide, ndi pangano losatha [Paska], ndipo tiyeneranso kudziwa dzina latsopano la Yesu. Malo amene Khristu Ahnsahnghong anabwezeretsera Paska wa pangano latsopano ndi Mpingo wa Mulungu.
119 Bundang P.O.Box, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Rep. of KOREA
Tel 031-738-5999 Fax 031-738-5998
Likulu la Ofesi: 50, Sunae-ro, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Dziko la Korea
Mpingo Waukulu: 35, Pangyoyeok-ro, Bundang-gu, Seongnam-si, Gyeonggi-do, Dziko la Korea
ⓒ Gulu la Utumiki wa Dziko Lonse la Mpingo wa Mulungu. Ma Umwini onse ndi Otetezedwa Mfundo za Zinsinsi